Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • mwb17.12 4
  • December 18-24

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • December 18-24
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17.12 4

December 18-24

ZEKARIYA 9-14

  • Nyimbo Na. 49 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Musachoke ‘M’chigwa cha Pakati pa Mapiri’”: (10 min.)

    • Zek. 14:3, 4​—“Chigwa chachikulu kwambiri” chikuimira chitetezo chochokera kwa Mulungu (w13 2/15 19 ¶10)

    • Zek. 14:5​—Anthu amene ‘angathawire m’chigwachi’ adzatetezedwa (w13 2/15 20 ¶13)

    • Zek. 14:6, 7, 12, 15​—Anthu amene ali kunja kwa chigwa cha Yehova cha chitetezo adzawonongedwa (w13 2/15 20 ¶15)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Zek. 12:3​—Kodi Yehova anasandutsa bwanji Yerusalemu kukhala “mwala wotopetsa”? (w07 12/15 22-23 ¶9-10)

    • Zek. 12:7​—N’chifukwa chiyani Yehova adzayambirire kupulumutsa “mahema a Yuda”? (w07 12/15 25 ¶13)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Zek. 12:1-14

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) g17.6 14-15​—Muitanireni kumisonkhano yathu.

  • Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) g17.6​—tsamba 14 ndi 15. Sonyezani mmene mungapangire ulendo wobwereza pogwiritsa ntchito magazini imene munamusiyira pa ulendo woyamba. Kenako muitanireni kumisonkhano yathu.

  • Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) jl phunziro 5​—Muitanireni kumisonkhano yathu.

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 98

  • Zimene Gulu Lathu Lachita: (7 min.) Onetsani vidiyo yakuti Zimene Gulu Lathu Lachita ya December.

  • “Mbali Yatsopano pa Misonkhano ya Mkati mwa Mlungu”: (8 min.) Nkhani yokambirana. Onetsani vidiyo ya Betefage, Phiri la Maolivi ndi Yerusalemu.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) kr mutu 11 ¶22-28 komanso tsamba 117

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 5 ndi Pemphero

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani