Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • mwb18.12 2
  • December 3-9

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • December 3-9
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18.12 2

December 3-9

MACHITIDWE 9-11

  • Nyimbo Na. 115 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Munthu Amene Ankazunza Akhristu Anakhala Mkhristu Wakhama”: (10 min.)

    • Mac. 9:1, 2​—Saulo ankazunza kwambiri ophunzira a Yesu (bt 60 ¶1-2)

    • Mac. 9:15, 16​—Saulo anasankhidwa kuti azichitira umboni za Yesu (w16.06 7 ¶4)

    • Mac. 9:20-22​—Saulo anakhala Mkhristu wakhama (bt 64 ¶15)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Mac. 9:4​—N’chifukwa chiyani Yesu anafunsa Saulo kuti: “N’chifukwa chiyani ukundizunza?” (bt 60-61 ¶5-6)

    • Mac. 10:6​—N’chifukwa chiyani n’zochititsa chidwi kuti mtumwi Petulo ankakhala kunyumba kwa munthu wofufuta zikopa? (“Simoni, wofufuta zikopa” mfundo zimene ndikuphunzira pa Mac. 10:6, nwtsty)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Mac. 9:10-22

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Woyamba: (4 min.) Onerani ndi kukambirana mfundo za m’vidiyoyi.

  • Ulendo Wobwereza Woyamba: (Osapitirira 3 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha ulendo wobwereza woyamba.

  • Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) jl mutu 6

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 58

  • Zofunika Pampingo: (8 min.)

  • Zimene Gulu Lathu Lachita: (7 min.) Onetsani vidiyo ya Zimene Gulu Lathu Lachita ya December.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 16

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 73 ndi Pemphero

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani