Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • sjj 154
  • Chikondi Sichitha

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chikondi Sichitha
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Musalole Kuti Chikondi Chanu Chizirale
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj 154

NYIMBO 154

Chikondi Sichitha

zosindikizidwa

(1 Akorinto 13:8)

  1. 1. Tangoonani

    Timakondanadi

    Zomwe n’zosowa m’dzikoli.

    Ndi anzathuwa

    Tikusangalala,

    Sitili mbali ya dziko.

    (KUKONZEKERA KOLASI)

    Chikondi sichithadi.

    Chimapiriratu.

    (KOLASI)

    Chikondichitu,

    Yehova n’chikondi.

    Watipatsa.

    Chikondichitu,

    Ndi chofunikadi.

    Tizikondanabe,

    Ndipo tisasiye

    Chikondichi.

  2. 2. Pena mavuto

    Angatifo’ketse

    N’kuvutika kupirira,

    Koma kupatsa

    Ndi kosangalatsa,

    M’lungu amatitonthoza.

    (KUKONZEKERA KOLASI)

    Chikondi sichithadi.

    Chimapiriratu.

    (KOLASI)

    Chikondichitu,

    Yehova n’chikondi.

    Watipatsa.

    Chikondichitu,

    Ndi chofunikadi.

    Tizikondanabe,

    Ndipo tisasiye.

    (KOLASI)

    Chikondichitu,

    Yehova n’chikondi.

    Watipatsa.

    Chikondichitu,

    Ndi chofunikadi.

    Tizikondanabe,

    Ndipo tisasiye

    Chikondichi,

    Chikondichi,

    Chikondichi.

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani