Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • mwb23.03 12
  • “Uteteze Mtima Wako”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Uteteze Mtima Wako”
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Nkhani Yofanana
  • Zosankha Zomwe Zimasonyeza Kuti Timadalira Yehova
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Mupeze Mayankho a Mafunso Awa
    Pulogalamu ya Msonkhano Wadera Wokhala ndi Woimira Nthambi wa 2025-2026
  • Mupeze Mayankho a Mafunso Awa
    Pulogalamu ya Msonkhano Wadera Wokhala ndi Woyang’anira Dera wa 2025-2026
  • Muziwerenga Baibulo Tsiku Lililonse Komanso Muzifunafuna Nzeru
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
mwb23.03 12

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

“Uteteze Mtima Wako”

Yehova anauzira Solomo kulemba kuti: “Uteteze mtima wako kuposa zonse zimene ziyenera kutetezedwa.” (Miy 4:23) Koma n’zomvetsa chisoni kuti Aisiraeli omwe anali anthu a Mulungu anasiya kutumikira Yehova “ndi mtima wawo wonse.” (2Mb 6:14) Ngakhale Mfumu Solomo inalola kuti akazi omwe sankalambira Yehova apotoze mtima wake n’kuyamba kulambira milungu ina. (1Mf 11:4) Kodi tingateteze bwanji mtima wathu? Nkhaniyi ili mu Nsanja ya Olonda yophunzira ya January 2019, tsamba 14-19.

ONERANI VIDIYO YAKUTI ZIMENE TINAPHUNZIRA MU NSANJA YA OLONDA​—KODI TINGATETEZE BWANJI MTIMA WATHU?, KENAKO YANKHANI MAFUNSO OTSATIRAWA:

Kodi n’chiyani chimene chikanafooketsa chikhulupiriro cha Akhristuwa, nanga nkhani yophunzirayi inawathandiza bwanji kuteteza mtima wawo?

  • Brent and Lauren

    Chithunzi cha muvidiyo yakuti “Zimene Tinaphunzira mu Nsanja ya Olonda​—Kodi Tingateteze Bwanji Mtima Wathu?” Brent ndi Lauren akufotokoza zimene zinawachitikira.
  • Umjay

    Chithunzi cha muvidiyo yakuti “Zimene Tinaphunzira mu Nsanja ya Olonda​—Kodi Tingateteze Bwanji Mtima Wathu?” Umjay akuona zithunzi za malo enaake.
  • Happy Layou

    Chithunzi cha muvidiyo yakuti “Zimene Tinaphunzira mu Nsanja ya Olonda​—Kodi Tingateteze Bwanji Mtima Wathu?” Happy akufotokoza zimene zinamuchitikira.

Kodi nkhani yophunzira imeneyi inakuthandizani bwanji?

    Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
    • tumizirani
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • zachinsinsi
    • JW.ORG
    • Lowani
    tumizirani