Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano

Mawu a M'munsi

g Kuyambira pamenepa, Saulo anayamba kutchedwa kuti Paulo. Ena amanena kuti Saulo anasankha dzina la Chiroma limeneli popereka ulemu kwa Serigio Paulo. Komabe, Saulo anapitiriza kugwiritsa ntchito dzina lakuti Paulo ngakhale atachoka ku Kupuro, ndipo zimenezi zikusonyeza kuti Paulo, amene anali “mtumwi wotumidwa kwa anthu a mitundu ina,” anaganiza zosintha dzina lakeli kuti azidziwika ndi dzina la Chiroma. Iye ayenera kuti anasankha dzina lakuti Paulo chifukwa chakuti katchulidwe ka dzina la Chiheberi lakuti Saulo, m’Chigiriki kamafanana ndi katchulidwe ka mawu ena otukwana.​—Aroma 11:13.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani