Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano

Mawu a M'munsi

a Kulapa kwenikweni kumaphatikizapo zambiri, osati kungonena kuti tikudzimvera chisoni chifukwa cha tchimo limene tachita. Pogwiritsa ntchito zitsanzo za Mfumu Ahabu, Mfumu Manase ndi mwana wolowerera wa m’fanizo la Yesu, nkhaniyi itithandiza kumvetsa zimene kulapa kwenikweni kumatanthauza. Tionanso mfundo zimene akulu ayenera kuganizira kuti adziwe ngati Mkhristu amene anachita tchimo lalikulu akusonyeza kulapa kwenikweni.

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani