Mawu a M'munsi
a Baibulo limanena kuti anthu ena sadzakhululukidwa. Anthu amenewa amakhala kuti asankha kuti nthawi zonse azitsutsana ndi Mulungu. Ndi Yehova kapena Yesu yekha amene amadziwa kuti munthu ndi wosayenera kumukhululukira.—Maliko 3:29; Aheb. 10:26, 27.