LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 128
  • Zochitika za Padzikoli Zikusintha

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zochitika za Padzikoli Zikusintha
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Ufumu Ulamulila—Ubwele!
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Mulungu Watilonjeza Moyo Wosatha
    Imbirani Yehova
  • Lonjezo la Moyo Wamuyaya
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • ‘Tsimikizilani Zinthu Zofunika Kwambili’
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 128

Nyimbo 128

Zochitika za Padzikoli Zikusintha

(1 Akorinto 7:31)

1. Mulungu anapereka

Mwana wake mmodzi yekha

Kuti zikhale zotheka

Kudzapulumutsidwa.

(KOLASI)

Ngakhale dzikoli

likusintha

Mulungu adzadalitsa

Dzikoli ndi kumwamba.

2. Dzikolitu likudwala

Kuvutika ndi kofala

Koma tikusangalala

Ufumu unabadwa.

(KOLASI)

Ngakhale dzikoli

likusintha

Mulungu adzadalitsa

Dzikoli ndi kumwamba.

(Onaninso Sal. 115:15, 16; Aroma 5:15-17; 7:25; Chiv. 12:5.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani