LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • rj tsa. 16
  • Kumapeto

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kumapeto
  • Bwelelani kwa Yehova
Bwelelani kwa Yehova
rj tsa. 16

Kumapeto

Kodi nthawi zina mumakumbukila mmene munali kusangalalila ndi anthu a Yehova kapena mmene munasangalalila kwambili ndi msonkhano wina wa mpingo? Kodi mumakumbukilanso msonkhano wacigawo wosaiŵalika umene munapezekapo, zinthu zabwino zimene zinakucitikilani mu ulaliki, kapena makambilano olimbikitsa amene munali nao ndi Mkristu mnzanu? Ngati mumatelo, ndiye kuti simunaiŵale Yehova, ndipo nayenso sanakuiŵaleni. Iye sanaiŵale zimene munali kucita pom’tumikila, ndipo ndi wofunitsitsa kukuthandizani kubwelela kwa iye.

Yehova akuti: “Inetu ndidzafunafuna nkhosa zanga ndi kuzisamalila. Ndidzasamalila nkhosa zanga ngati mmene amacitila munthu amene amadyetsa gulu la nkhosa zake pamene ali pakati pa nkhosa zimene zinabalalika . . . ndidzapulumutsa nkhosazo kucokela m’malo onse kumene zinabalalikila.”—Ezekieli 34:11, 12.

Cithunzi coonetsa alongo acimwemwe pa msonkhano wacigawo
    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani