LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • lfb masa. 4-5
  • Zamkati

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zamkati
  • Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
lfb masa. 4-5

Zamkati

Nchito Yolenga Zinthu

1 Mulungu Anapanga Kumwamba na Dziko Lapansi

2 Mulungu Anapanga Mwamuna na Mkazi Oyamba

Kucokela pa Adamu Mpaka pa Cigumula ca Nowa

3 Adamu na Hava Sanamvele Mulungu

4 Kukwiya Mpaka Kupha Munthu

5 Cingalawa ca Nowa

6 Anthu 8 Anapulumuka na Kuloŵa m’Dziko Latsopano

Kucokela pa Cigumula ca Nowa Mpaka pa Yakobo

7 Nsanja ya Babele

8 Abulahamu na Sara Anamvela Mulungu

9 Mpaka Anakhala na Mwana Wake!

10 Kumbukilani Mkazi wa Loti

11 Cikhulupililo Ciyesedwa

12 Yakobo Analandila Coloŵa

13 Yakobo na Esau Akhalanso pa Mtendele

Kucokela pa Yosefe Mpaka pa Kuwoloka Nyanja Yofiila 38

14 Kapolo Amene Anamvela Mulungu

15 Yehova Sanamuiŵalepo Yosefe

16 Kodi Yobu Anali Ndani?

17 Mose Anasankha Kulambila Yehova

18 Citsamba Coyaka Moto

19 Milili Itatu Yoyambilila

20 Milili 6 Yokonkhapo

21 Mlili wa Namba 10

22 Cozizwitsa pa Nyanja Yofiila

Mu Cipululu

23 Lonjezo kwa Yehova

24 Sanasunge Lonjezo

25 Cihema Colambililako

26 Azondi 12

27 Anapandukila Yehova

28 Bulu wa Balamu Akamba

Nthawi ya Oweluza

29 Yehova Asankha Yoswa

30 Rahabi Abisa Azondi

31 Yoswa na Agibeoni

32 Mtsogoleli Watsopano na Azimayi Aŵili Olimba Mtima

33 Rute na Naomi

34 Gidiyoni Agonjetsa Amidiyani

35 Hana Apemphela Kuti Akhale na Mwana

36 Lonjezo la Yefita

37 Yehova Akamba na Samueli

38 Yehova Anapatsa Samsoni Mphamvu

Davide na Sauli

39 Mfumu Yoyamba ya Aisiraeli

40 Davide na Goliyati

41 Davide na Sauli

42 Yonatani, Munthu Wolimba Mtima Komanso Wokhulupilika

43 Chimo la Mfumu Davide

Kucokela pa Solomo Mpaka pa Nthawi ya Eliya 106

44 Kacisi wa Yehova

45 Ufumu Ugaŵika

46 Mulungu Woona Adziŵika pa Phili la Karimeli

47 Yehova Alimbikitsa Eliya

48 Mwana wa Mkazi Wamasiye Aukitsidwa

49 Mfumukazi Yoipa Inalangiwa

50 Yehova Ateteza Yehosafati

Kucokela pa Elisa Mpaka pa Nthawi ya Yosiya

51 Kamtsikana Kathandiza Mkulu wa Asilikali

52 Asilikali a Yehova Amoto

53 Yehoyada Anali Wolimba Mtima

54 Yehova Anamulezela Mtima Yona

55 Mngelo wa Yehova Ateteza Hezekiya

56 Yosiya Anali Kukonda Cilamulo ca Mulungu

Kucokela pa Yeremiya Mpaka pa Nthawi ya Nehemiya

57 Yehova Atumiza Yeremiya Kuti Akalalikile

58 Yerusalemu Awonongedwa

59 Anyamata Anayi Amene Anamvela Yehova

60 Ufumu Umene Udzalamulila Kwamuyaya

61 Anakana Kugwadila Fano

62 Ufumu Woimilidwa na Mtengo Waukulu

63 Dzanja Lilemba pa Cipupa

64 Danieli Anaponyedwa m’Dzenje la Mikango

65 Esitere Apulumutsa Anthu a Mtundu Wake

66 Ezara Aphunzitsa Cilamulo ca Mulungu

67 Mpanda wa Yerusalemu Umangidwanso

Yohane M’batizi na Yesu

68 Elizabeti Akhala na Mwana

69 Gabirieli Aonekela kwa Mariya

70 Angelo Alengeza za Kubadwa kwa Yesu

71 Yehova Anateteza Yesu

72 Pamene Yesu Anali Wacicepele

73 Yohane Anakonza Njila

Utumiki wa Yesu

74 Pamene Yesu Anakhala Mesiya

75 Mdyelekezi Ayesa Yesu

76 Yesu Ayeletsa Kacisi

77 Mzimayi Akumana na Yesu pa Citsime

78 Yesu Analalikila Uthenga wa Ufumu

79 Yesu Acita Zozizwitsa Zambili

80 Yesu Asankha Atumwi 12

81 Ulaliki wa pa Phili

82 Yesu Anaphunzitsa Otsatila Ake Kupemphela

83 Yesu Adyetsa Khamu la Anthu

84 Yesu Anayenda pa Madzi

85 Yesu Acilitsa pa Sabata

86 Yesu Aukitsa Lazaro

Wiki ya Yesu Yothela pa Dziko Lapansi

87 Mgonelo wa Ambuye 204

88 Am’gwila Yesu

89 Petulo Akana Yesu

90 Yesu Aphedwa ku Gologota

91 Yesu Aukitsidwa

92 Yesu Aonekela kwa Ophunzila Ake Asodzi

93 Yesu Abwelela Kumwamba

Cikhristu Cifalikila ku Madela Ena

94 Ophunzila a Yesu Alandila Mzimu Woyela

95 Palibe Akanawaletsa Kulalikila

96 Yesu Asankha Saulo

97 Koneliyo Alandila Mzimu Woyela

98 Cikhristu Cifalikila ku Madela Akutali

99 Woyang’anila Ndende Aphunzila Coonadi

100 Paulo na Timoteyo

101 Paulo Atumizidwa ku Roma

102 Masomphenya a Yohane

103 “Ufumu Wanu Ubwele”

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani