LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 89
  • Mvela Udalitsike

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Mvela Udalitsike
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Khalani Omvera Kuti Mulandire Madalitso
    Imbirani Yehova
  • Kodi Ndinu ‘Wokonzeka Kumvela’?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2023
  • Ni Moyo Wawo
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Ni Moyo Wawo
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 89

NYIMBO 89

Mvela Udalitsike

Yopulinta

(Luka 11:28)

  1. 1. Ngati timamveladi Yesu Khristu.

    Tidzacita zimene anena.

    Tikacita zimene tiphunzila,

    Tidzakondwa tidzadalitsidwa.

    (KOLASI)

    Ukamvela Yehova,

    Udzasangalaladi.

    Ukacita zimene anena,

    Udzadalitsidwadi.

  2. 2. Monga nyumba yomangidwa pathanthwe

    Osati yomangidwa pamcenga.

    Titsatile citsogozo ca Yesu,

    Tidzalimba ndipo sitingagwe.

    (KOLASI)

    Ukamvela Yehova,

    Udzasangalaladi.

    Ukacita zimene anena,

    Udzadalitsidwadi.

  3. 3. Mtengo wobyalidwa m’mbali mwa madzi

    Umabala nthawi ikafika,

    Tizimvela monga ana a M’lungu,

    Ndipo Yehova ‘dzatidalitsa.

    (KOLASI)

    Ukamvela Yehova,

    Udzasangalaladi.

    Ukacita zimene anena,

    Udzadalitsidwadi.

(Onaninso Deut. 28: 2, Sal. 1:3; Miy. 10:22; Mat. 7: 24-27; Luka 6:47-49.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani