LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w17 April tsa. 2
  • Zamkati

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zamkati
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
w17 April tsa. 2

Zamkati

WIKI YA MAY 29, 2017–JUNE 4, 2017

3 ‘Muzikwanilitsa Zimene Mwalonjeza’

Kodi munapangapo malonjezo angati kwa Yehova? Limodzi, aŵili, kapena ambili? Kodi mumayesetsa kucita zinthu mogwilizana ndi malonjezo anu? Nanga bwanji ponena za lonjezo lanu la kudzipeleka kapena la cikwati? Nkhani ino, idzatikumbutsa citsanzo cabwino cimene Yefita ndi Hana anatipatsa pamene tiyesetsa kukwanilitsa zimene tinalonjeza kwa Mulungu.

WIKI YA JUNE 5-11, 2017

9 Kodi Cidzacokapo N’ciani Ufumu wa Mulungu Ukadzabwela?

Nthawi zambili timaganizila zimene Yehova adzaticitila m’Paradaiso. Koma m’nkhani ino, tidzakambilana zimene Mulungu adzacotsa padziko lapansi. Kodi Yehova adzacotsa ciani kuti padziko pakhale mtendele ndi cimwemwe? Kuganizila yankho la funso limeneli, kudzalimbitsa cikhulupililo cathu ndi kutithandiza kukhalabe opilila.

14 Mbili Yanga—N’natsimikiza Mtima Kukhala Msilikali wa Khristu

WIKI YA JUNE 12-18, 2017

18 Woweluza wa Dziko Lonse” Amacita Cilungamo Nthawi Zonse

WIKI YA JUNE 19-25, 2017

23 Kodi Mumacita Zinthu Mogwilizana ndi Cilungamo ca Yehova?

Tikaona kuti ife kapena munthu wina wacitilidwa zinthu zopanda cilungamo, cikhulupililo, kudzicepetsa, ndi kukhulupilika kwathu zingayesedwe. Nkhanizi zidzafotokoza zocitika zitatu za m’Baibo, zimene zidzatithandiza kucita zinthu mogwilizana ndi cilungamo ca Yehova.

WIKI YA JUNE 26, 2017–JULY 2, 2017

28 Yehova Atamandike Cifukwa ca Kudzipeleka Kwanu!

Yehova payekha ni wacikwane-kwane. Komabe, iye amakondwela akaona kuti tikuyesetsa kucilikiza ulamulilo wake. Oweruza macaputa 4 ndi 5, aonetsa kuti Yehova amayamikila ngati ticita modzipeleka zimene iye watilamula.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani