LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w18 August tsa. 2
  • ZAMKATI

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • ZAMKATI
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2018
w18 August tsa. 2

ZAMKATI

WIKI YA OCTOBER 1-7, 2018

3 Kodi Mudziŵa Bwino Zoona Zake?

WIKI YA OCTOBER 8-14, 2018

8 Musamaweluze Poona Maonekedwe Akunja

M’nkhani yoyamba, tidzakambilana zinthu zimene zingapangitse kuti cikhale covuta kudziŵa zoona zeni-zeni pa nkhani inayake imene tamva. Tidzakambilananso mfundo za m’Baibo zimene zingatithandize kukulitsa luso lopenda mosamala nkhani imene tamva kuti tidziŵe ngati ni ya zoona. M’nkhani yaciŵili, tidzakambilana zinthu zitatu zimene nthawi zambili anthu amaziona monga maziko oweluzila anzawo potengela maonekedwe akunja. Tidzakambilananso zimene zingatithandize kukulitsa mtima wopanda tsankho pocita zinthu na ena.

13 Mbili Yanga​—N’natsimikiza Mtima Kuti Sinidzabwelela M’mbuyo

WIKI YA OCTOBER 15-21, 2018

18 Opatsa Mowoloŵa Manja Amakhala Acimwemwe

WIKI YA OCTOBER 22-28, 2018

23 Muziseŵenza na Yehova Tsiku Lililonse

Yehova analenga anthu kuti akhale na umoyo wabwino komanso wacimwemwe. Timakhala na umoyo wacimwemwe ngati tiseŵenza na Yehova tsiku lililonse pokwanilitsa cifunilo cake. M’nkhani ziŵili zimenezi, tidzakambilana mapindu amene timapeza tikamaonetsa kuolowa manja m’njila zosiyana-siyana.

28 Kuleza Mtima Kumatanthauza Kupilila Tili na Colinga

31 Za M’nkhokwe Yathu

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani