LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 12/14 tsa. 8
  • Zilengezo

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zilengezo
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
km 12/14 tsa. 8

Zilengezo

◼ December: Gaŵilani buku la mutu wakuti Zimene Baibo Imaphunzitsa M’ceni-ceni kapena gaŵilani kalikonse ka tumapepala twauthenga utu: Kodi Baibo Mumaiona Bwanji?, Kodi Zinthu Zidzakhala Bwanji Mtsogolo?, Kodi Cofunika N’ciani Kuti Banja Likhale Lamtendele?, Kodi Ndani Maka-maka Amene Akulamulila Dzikoli?, Kodi Mavuto Adzathadi?, ndi kakuti Kodi N’zoona Kuti Akufa Angakhalenso ndi Moyo? January ndi February: Gaŵilani kabuku kakuti, Uthenga Wabwino Wocokela kwa Mulungu. March: Gaŵilani magazini a Nsanja ya Mlonda ndi Galamukani!

◼ Cikumbutso ca mu 2016 cidzacitika pa Citatu pa March 23, 2016.

◼ Kuyambila pa January 1, 2015, makonzedwe akuti mipingo iziyambitsa maphunzilo a Baibulo pa Ciŵelu coyamba ca mwezi adzatha. M’malomwake, ofalitsa adzayamba kugaŵila magazini monga mmene timacitila pa Ciŵelu ciliconse. Tingayambitse maphunzilo a Baibulo nthawi iliyonse m’mweziwo pogwilitsila nchito magazini kapena mabuku ena ogwilitsila nchito pophunzila.

◼ Zofalitsa Zatsopano Zimene Zilipo:

Vidiyo yakuti Jehovahs Witnesses Organised to share the good news ndi yakuti Our Whole Association Of Brothers—Cimambwe-Lungu.

Buku Lapacaka la Mboni za Yehova la 2015—Cikikaonde

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani