LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb16 May tsa. 7
  • May 30–June 5

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • May 30–June 5
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
mwb16 May tsa. 7

May 30–June 5

SALIMO 26-33

  • Nyimbo 23 ndi Pemphelo

  • Mau Oyamba (Mph. 3 kapena zocepelapo)

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU

  • “Dalilani Yehova Kuti Akulimbitseni Mtima”: (Mph. 10)

    • Sal. 27:1-3—Kuganizila mmene Yehova wakhalila kuwala kwathu kungatithandize kukhala wolimba mtima (w12-CN 7/15 22-23 ndime 3-6)

    • Sal. 27:4—Kukonda kulambila koona kumatithandiza kukhala wolimba mtima. (w12-CN 7/15 24 ndime 7)

    • Sal. 27:10—Yehova ndi wokonzeka kuthandiza atumiki ake pamene ena awasala. (w12-CN 7/15 24 ndime 9-10)

  • Kufufuza Cuma Cakuuzimu: (Mph. 8)

    • Sal. 26:6—Mofanana ndi Davide, kodi tingazungulile motani guwa la nsembe la Yehova? (w06-CN 5/15 19 ndime 11)

    • Sal. 32:8—Ndi mapindu otani amene timapeza tikamalandila malangizo ocokela kwa Yehova? (w09-CN 6/1 5 ndime 3)

    • Kodi kuŵelenga Baibulo kwa mlungu uno kwandiphunzitsa ciani za Yehova?

    • Ndi mfundo ziti pa kuŵelenga Baibulo kwa mlungu uno zimene ndingagwilitsile nchito mu ulaliki?

  • Kuŵelenga Baibulo: (Mph. 4 kapena zocepelapo) Salimo 32:1–33:8

KUONJEZELA LUSO LANU MU ULALIKI

  • Ulendo Woyamba: (Mph. 2 kapena zocepelapo) kt—Ŵelengani lemba pa cipangizo cokhala ndi intaneti.

  • Ulendo Wobwelelako: (Mph. 4 kapena zocepelapo) Citani citsanzo coonetsa mmene tingayambitsile phunzilo la Baibulo kwa munthu amene timam’gaŵila magazini mwa kumuonetsa vidiyo yakuti N’ciani Cimacitika pa Phunzilo la Baibulo? pa JW Laibulale.

  • Phunzilo la Baibulo: (Mph. 6 kapena zocepelapo) jl phunzilo 9—Mwacidule wofalitsa aonetse wophunzila mmene angagwilitsile nchito JW Laibulale pokonzekela misonkhano.

UMOYO WATHU WACIKRISTU

  • Nyimbo 130

  • Zosoŵa za pampingo: (Mph. 15) Ngati mufuna, kambilanani zimene mwaphunzilapo pa nkhani za m’Buku Lapacaka. (yb16 masamba 112-113; ndi masamba 135-136)

  • Phunzilo la Baibulo la Mpingo: (Mph. 30) ia mutu 16 ndime 16-29, bokosi pa tsa. 142, ndi kubwelelamo pa tsa. 144

  • Kubweleza Mfundo Zimene Taphunzila ndi Kufotokoza Zomwe Tidzaphunzila Mlungu Wotsatila (Mph. 3)

  • Nyimbo 16 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani