LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb16 October tsa. 3
  • October 10-16

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • October 10-16
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
mwb16 October tsa. 3

October 10-16

MIYAMBO 7–11

  • Nyimbo 32 na Pemphelo

  • Mau Oyamba (Mph. 3 kapena zocepelapo)

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU

  • “Mtima Wako Usapatuke” (Mph. 10)

    • Miy. 7:6-12—Anthu opanda nzelu mumtima mwawo amawononga umoyo wawo wauzimu (w00 11/15 CN, tsa 29-30)

    • Miy. 7:13-23—Kusankha zocita mopanda nzelu kumabweletsa mavuto (w00 11/15 CN, tsa. 30-31)

    • Miy. 7:4, 5, 24-27—Nzelu ndi kumvetsa zinthu kumatiteteza (w00 11/15 CN, tsa. 29, 31)

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (Mph. 8)

    • Miy. 9:7-9—Kodi zimene timacita tikapatsidwa uphungu zimaonetsa kuti ndife anthu a bwanji? (w01 5/15-CN, tsa. 29-30)

    • Miy. 10:22—Ndi madalitso a Yehova ati amene timalandila masiku ano? (w06 5/15 CN, tsa. 26-30 ndime 3-16)

    • Kuŵelenga Baibulo kwa mlungu uno kwaniphunzitsa ciani za Yehova?

    • Ni mfundo ziti pa kuŵelenga Baibulo kwa mlungu uno zimene ningaseŵenzetse mu ulaliki?

  • Kuŵelenga Baibulo: (Mph. 4 kapena zocepelapo) Miy. 8:22–9:6

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Ulendo Woyamba: (Mph. 2 kapena zocepelapo) g16.5 nkhani ya pacikuto—Itanilani munthuyo ku misonkhano ya kumapeto kwa mlungu.

  • Ulendo Wobwelelako: (Mph. 4 kapena zocepelapo) g16.5 nkhani ya pacikuto—Itanilani munthuyo ku misonkhano ya kumapeto kwa mlungu.

  • Phunzilo la Baibulo: (Mph. 6 kapena zocepelapo) bh tsa. 176 ndime 5-6—Itanilani wophunzilayo ku misonkhano.

UMOYO WATHU WACIKHIRISTU

  • Nyimbo 83

  • Zimene Acicepele Anzanu Amakamba—Mafoni (Miy. 10:19): (Mphi. 15) Kukambilana. Yambani mwa kutambitsa vidiyo yakuti Zimene Acicepele Anzanu Amakamba—Mafoni, ngati ilipo. Ndiyeno kambilanani nkhani ya pa jw.org yakuti “Kodi Ndiyenera Kudziwa Zotani Zokhudza Mameseji a Pafoni?” Nkhaniyi mungaipeze pa webusaiti m’Chichewa. Gogomezani mfundo zimene zili pa kamutu kakuti “Zofunika kukumbukira pa nkhani ya mameseji.”

  • Phunzilo la Baibulo la Mpingo: (Mph. 30) kr nkhani 2 ndime 13-22

  • Kubwelelamo ndi Kuchulako za Mlungu Wotsatila (Mph. 3)

  • Nyimbo 152 na Pemphelo

    Cikumbutso: Lizani nyimboyi kamodzi, pambuyo pake mpingo wonse uyimbile pamodzi

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani