LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb17 June tsa. 2
  • June 5-11

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • June 5-11
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
mwb17 June tsa. 2

June 5-11

YEREMIYA 51-52

  • Nyimbo 37 na Pemphelo

  • Mau Oyamba (3 mineti kapena kucepelapo)

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU

  • “Mau Onse a Yehova Amakwanilitsika”: (10 min.)

    • Yer. 51:11, 28—Yehova anakambilatu amene adzagonjetsa Babulo (it-2 peji 360 mapa. 2-3)

    • Yer. 51:30—Yehova anakambilatu kuti Babulo sadzadziteteza pogonjetsedwa (it-2 peji 459 pala. 4)

    • Yer. 51:37, 62—Yehova anakambilatu za kuwonongeka kothelatu kwa Babulo (it-1 peji 237 pala. 1)

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (8 min.)

    • Yer. 51:25—N’cifukwa ciani Babulo amamucha kuti “phili lowononga”? (it-2 peji 444 pala. 9)

    • Yer. 51:42—Kodi mau akuti “Nyanja yasefukila ndi kumiza Babulo” atanthauza ciani? (it-2 peji 882 pala. 3)

    • Kodi imwe pacanu kuŵelenga Baibo kwa wiki ino kwakuphunzitsani ciani za Yehova?

    • Ni cuma ca kuuzimu cina citi cimene mwapeza pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino?

  • Kuŵelenga Baibo: (4 mineti kapena kucepelapo) Yer. 51:1-11

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Konzekelani Maulaliki a Mwezi Uno: (15 min.) Kukambilana “Maulaliki a Citsanzo.” Tambitsani vidiyo imodzi-imodzi ndipo kambilanani zimene mwaphunzilapo. Limbikitsani ofalitsa kuonetsa mwininyumba zili pa jw.org ku Chichewa polemba kuti ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA > MALANGIZO OTHANDIZA BANJA LONSE.

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

  • Nyimbo 152

  • “Kodi Cikhulupililo Canu m’Malonjezo a Yehova N’colimba Bwanji?”: (15 min.) Mafunso na mayankho. Limbikitsani onse kuti nthawi ndi nthawi azikambilana maulosi a m’Baibo na okhulupilila anzawo n’colinga colimbikitsana cikhulupililo.—Aroma 1:11, 12.

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) kr nkhani 13 mapa. 24-32

  • Kubwelelamo na Kuchulako za Wiki Yotsatila (3 min.)

  • Nyimbo 49 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani