LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb17 August tsa. 7
  • August 28–September 3

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • August 28–September 3
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
mwb17 August tsa. 7

August 28–September 3

EZEKIELI 39-41

  • Nyimbo 107 na Pemphelo

  • Mau Oyamba (3 mineti kapena kucepelapo)

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU

  • “Mmene Masomphenya a Ezekieli a Kacisi Amakukhudzilani”: (10 min.)

    • Ezek. 40:2—Kulambila Yehova n’kokwezeka kwambili kuposa kulambila kwina kulikonse (w99 3/1 peji 11 pala. 16)

    • Ezek. 40:3, 5—Mosakaikila, Yehova adzakwanilitsa cifunilo cake cokhudza kulambila koyela (w07 8/1 peji 10 pala. 2)

    • Ezek. 40:10, 14, 16—Tifunika kutsatila miyezo ya Yehova yapamwamba ndi yolungama kuti kulambila kwathu kukhale kovomelezeka (w07 8/1 peji 11 pala. 4)

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (8 min.)

    • Ezek. 39:7—N’cifukwa ciani tingati anthu akamaimba Mulungu mlandu cifukwa ca zopanda cilungamo zimene zicitika, ndiye kuti akudetsa dzina lake? (w12 9/1 peji 21 pala. 2)

    • Ezek. 39:9—Pambuyo pa Aramagedo, n’ciani cidzacitikila zida zomenyela nkhondo zimene anthu adzasiya? (w89 8/15 peji 14 pala. 20)

    • Kodi imwe pacanu, kuŵelenga Baibo kwa wiki ino kwakuphunzitsani ciani za Yehova?

    • Ni cuma ca kuuzimu cina citi cimene mwapeza pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino?

  • Kuŵelenga Baibo: (4 mineti kapena kucepelapo) Ezek. 40:32-47

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Ulendo Woyamba: (2 mineti kapena kucepelapo) fg phunzilo 1 pala. 1—Chulani za vidiyo yakuti Kodi Mungakonde Kumvelako Uthenga Wabwino? (koma musawatambitse) na kugaŵila kabuku.

  • Ulendo Wobwelelako: (4 mineti kapena kucepelapo) fg phunzilo 1 pala. 2—Yalani maziko a ulendo wotsatila.

  • Phunzilo la Baibo: (6 mineti kapena kucepelapo) fg phunzilo 1 mapa. 3-4

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

  • Nyimbo 145

  • “Ni Liti Pamene Ningadzacitekonso Upainiya Wothandiza?”: (15 min.) Kukambilana. Tambitsani vidiyo yakuti Cifukwa ca Thandizo la Yehova Ningakwanitse Kucita Ciliconse.

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) kr nkhani 17 mapa. 1-9

  • Kubwelelamo na Kuchulako za Wiki Yotsatila (3 min.)

  • Nyimbo 92 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani