LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb17 December tsa. 2
  • December 4-10

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • December 4-10
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano —2017
mwb17 December tsa. 2

December 4-10

ZEFANIYA 1–HAGAI 2

  • Nyimbo 27 na Pemphelo

  • Mau Oyamba (3 min. olo kucepelapo)

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU

  • “Funani Yehova Tsiku la Mkwiyo Wake Lisanafike”: (10 min.)

    • [Tambitsani vidiyo yakuti Mfundo Zokhudza Buku la Zefaniya.]

    • Zef. 2:2, 3—Funani Yehova, funani cilungamo, funani cifatso (w01 2/15 peji 18-19 mapa. 5-7)

    • [Tambitsani vidiyo yakuti Mfundo Zokhudza Buku la Hagai.]

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (8 min.)

    • Zef. 1:8—Kodi pavesili tipezapo cenjezo lanji? (w07 11/15 peji 11 pala. 3)

    • Hag. 2:9—Kodi ulemelelo wa kacisi wa Zerubabele unaposa bwanji uja wa kacisi wa Solomo? (w07 12/1 peji 9 pala. 3)

    • Kodi imwe pacanu, kuŵelenga Baibo kwa wiki ino kwakuphunzitsani ciani za Yehova?

    • Ni cuma ca kuuzimu cina citi cimene mwapeza pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino?

  • Kuŵelenga Baibo: (4 min. olo kucepelapo) Hag. 2:1-14

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Konzekelani Maulaliki a Mwezi Uno: (15 min.) Kukambilana “Maulaliki a Citsanzo.” Tambitsani na kukambilana mavidiyowo payokha-payokha. Limbikitsani ofalitsa kuti akagaŵile kwa anthu ambili Galamukani! Na. 6 2017. Popeza colinga cathu ndi kukambilana na anthu mwacindunji, tisamasiye magaziniyi panyumba imene palibe anthu.

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

  • Nyimbo 23

  • Zofunikila za Mpingo: (5 min.)

  • Cinenelo Coyela Cimalimbikitsa Mtendele na Mgwilizano (Zef. 3:9): (10 min.) Kukambilana kozikidwa pa Nsanja ya August 15, 2012, peji 12, pala. 4. Tambitsani vidiyo yakuti Anthu Amene Kale Anali Kuzondana Akhala Mabwenzi.

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) kr nkhani 22 mapa. 8-16

  • Kubwelelamo na Kuchulako za Wiki Yotsatila (3 min.)

  • Nyimbo 22 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani