LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb18 August tsa. 4
  • August 13-19

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • August 13-19
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
mwb18 August tsa. 4

August 13-19

LUKA 19-20

  • Nyimbo 84 na Pemphelo

  • Mau Oyamba (3 min. olo kucepelapo)

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU

  • “Phunzilamponi Kanthu pa Fanizo la Ndalama 10 za Mina”: (10 min.)

    • Luka 19:12, 13—“Munthu wina wa m’banja lacifumu” anauza akapolo ake kuti acite malonda mpaka iye atabwela (jy peji 232 mapa. 2-4)

    • Luka 19:16-19—Akapolo okhulupilika anali na maluso osiyana, koma aliyense wa iwo analandila mphoto (jy peji 232 pala. 7)

    • Luka 19:20-24—Kapolo woipa analephela kuseŵenza ndipo zinthu sizinamuyendele bwino (jy peji 233 pala. 1)

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (8 min.)

    • Luka 19:43—Kodi mau a Yesu amenewa anakwanilitsika bwanji? (“mpanda wazisonga” nwtsty mfundo younikila)

    • Luka 20:38—Kodi mau a Yesu amalimbitsa bwanji cikhulupililo cathu cakuti akufa adzauka? (“pakuti kwa iye onsewa ndi amoyo” nwtsty mfundo younikila)

    • Kodi imwe pacanu, kuŵelenga Baibo kwa wiki ino kwakuphunzitsani ciani za Yehova?

    • Ni cuma ca kuuzimu cina citi cimene mwapeza pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino?

  • Kuŵelenga Baibo: (4 min. olo kucepelapo) Luka 19:11-27

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Ulendo Woyamba: (2 min. olo kucepelapo) Seŵenzetsani makambilano acitsanzo.

  • Vidiyo ya Kubwelelako Koyamba: (5 min.) Tambitsani na kukambilana vidiyoyi.

  • Nkhani: (6 min. olo kucepelapo) w14 8/15 mape. 29-30—Mutu: Kodi Yesu pa Luka 20:34-36 Anali Kukamba za Ciukililo ca Padziko Lapansi?

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

  • Nyimbo 83

  • “Kunola Luso Lathu mu Ulaliki—Kuseŵenzetsa Webusaiti Yathu ya JW.ORG”: (15 min.) Kukambilana. Tambitsani vidiyoyi.

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 33

  • Kubwelelamo na Kuchulako za Wiki Yotsatila (3 min.)

  • Nyimbo 116 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani