LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb18 November tsa. 2
  • November 5-11

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • November 5-11
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
mwb18 November tsa. 2

November 5-11

YOHANE 20-21

  • Nyimbo 35 na Pemphelo

  • Mawu Oyamba (3 min. olo kucepelapo)

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Kodi Umandikonda Ine Kuposa Izi?”: (10 min.)

    • Yoh. 21:1-3—Pambuyo pa imfa ya Yesu, Petulo na ophunzila ena anapita kukasodza

    • Yoh. 21:4-14—Yesu ataukitsidwa, anaonekela kwa Petulo komanso kwa ophunzila ena

    • Yoh. 21:15-19—Yesu anathandiza Petulo kuona zimene afunika kuika patsogolo (“Yesu anafunsa Simoni Petulo”, “Kodi Umandikonda Ine Kuposa Izi?”, “kacitatu” nwtsty mfundo zounikila pa Yoh. 21:15, 17)

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (8 min.)

    • Yoh. 20:17—Kodi mawu amene Yesu anauza Mariya Mmagadala atanthauza ciani? (“Usandikangamile” nwtsty mfundo younikila)

    • Yoh. 20:28—N’cifukwa ciani Tomasi anatomola Yesu kuti “Mbuyanga ndi Mulungu wanga”? (“Mbuyanga ndi Mulungu wanga” nwtsty mfundo younikila)

    • Kodi imwe pacanu, kuŵelenga Baibo kwa wiki ino kwakuphunzitsani ciani za Yehova?

    • Ni cuma ca kuuzimu cina citi cimene mwapeza pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino?

  • Kuŵelenga Baibo: (4 min. olo kucepelapo) Yoh. 20:1-18

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Woyamba: (4 min.) Tambitsani na kukambilana vidiyoyi.

  • Kubwelelako Koyamba: (3 min. olo kucepelapo) Seŵenzetsani makambilano acitsanzo.

  • Phunzilo la Baibo: (6 min. olo kucepelapo) bhs peji 79 mapa. 21-22. Itanilani munthuyo ku misonkhano.

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

  • Nyimbo 37

  • Zofunikila za Mpingo: (15 min.)

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 42

  • Kubwelelamo na Kuchulako za Wiki Yotsatila (3 min.)

  • Nyimbo 45 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani