LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb18 November tsa. 3
  • November 12-18

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • November 12-18
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
mwb18 November tsa. 3

November 12-18

MACHITIDWE 1-3

  • Nyimbo 104 na Pemphelo

  • Mawu Oyamba (3 min. olo kucepelapo)

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Mzimu Woyela Unatsanulidwa pa Mpingo Wacikhristu”: (10 min.)

    • [Tambitsani vidiyo yakuti Mfundo Zokhudza Buku la Machitidwe.]

    • Mac. 2:1-8, 14, 37, 38, 41—Ophunzila a Yesu atalandila mzimu woyela analalikila uthenga wabwino. Zimenezi zinapangitsa kuti anthu pafupi-fupi 3,000 abatizike

    • Mac. 2:42-47—Ophunzila a Yesu anaonetsa khalidwe la kuwolowa manja komanso kuceleza kwakukulu. Izi zinathandiza kuti amene anali atangobatizika kumene akhalitseko ku Yerusalemu na kuti cikhulupililo cawo cilimbe.(w86 12/1 peji 29 mapa. 4-5, 7)

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (8 min.)

    • Mac. 3:15—N’cifukwa ciani Yesu akuchedwa “Mtumiki Wamkulu wa moyo”?(it-2 peji 61 pala. 1)

    • Mac. 3:19—Kodi vesiyi ionetsa kuti Yehova amawakhululukila bwanji ocimwa amene alapa? (cl peji 265 pala. 14)

    • Kodi imwe pacanu, kuŵelenga Baibo kwa wiki ino kwakuphunzitsani ciani za Yehova?

    • Ni cuma ca kuuzimu cina citi cimene mwapeza pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino?

  • Kuŵelenga Baibo: (4 min. olo kucepelapo) Mac. 2:1-21

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Ulendo Woyamba: (2 min. olo kucepelapo) Seŵenzetsani makambilano acitsanzo.

  • Vidiyo ya Kubwelelako Koyamba: (5 min.) Tambitsani na kukambilana vidiyoyi.

  • Nkhani: (6 min. olo kucepelapo) it-1 peji 129 mapa. 2-3—Mutu: N’cifukwa Ciani Yudasi Analoŵedwa M’malo Pamene Atumwi Ena Amene Anamwalila Ali Okhulupilika Sanaloŵedwe M’malo?

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

  • Nyimbo 85

  • “Kugwilizana Polalikila M’gawo la Vitundu Vosiyana-siyana”: (15 min.) Nkhani yokambilana yokambiwa na woyang’anila utumiki. Tambitsani na kukambilana vidiyoyi. Fotokozani makonzedwe amene alipo a mmene mudzalalikilila gawo la anthu okamba vitundu vosiyana-siyana.

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 43 mapa. 1-7

  • Kubwelelamo na Kuchulako za Wiki Yotsatila (3 min.)

  • Nyimbo 68 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani