LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb19 April tsa. 2
  • Umbeta ni Mphatso

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Umbeta ni Mphatso
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Nkhani Zofanana
  • Kodi Baibo Imati Ciyani pa Nkhani ya Umbeta na Ukwati?
    Kondwelani Na Moyo Kwamuyaya!—Maphunzilo a Baibo Okambilana Komanso Zocita
  • Lemekezani Wina Aliyense mu Mpingo
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2020
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
mwb19 April tsa. 2

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | 1 AKORINTO 7-9

Umbeta ni Mphatso

7:32, 35, 38

Kwa zaka zambili, Akhristu ambili amakamba kuti kukhala mbeta kuli na maubwino apadela. Kumawathandiza kuwonjezela utumiki, kupeza mabwenzi osiyana-siyana, komanso kuyandikila kwambili Yehova.

Abale atatu osakwatila ali pa ulendo wokalalikila ku Australia mu 1937; mlongo wosakwatiwa afika ku Mexico, ku nchito yake ya umishonale mu 1947

Ali pa ulendo wokalalikila ku Australia, mu 1937; Wotsiliza sukulu ya Giliyadi afika ku Mexico, kumene anatumizidwa, mu 1947

M’bale wosakwatila alalikila ku Brazil; mbeta zicita Sukulu ya Alengezi a Ufumu ku Malawi

Alalikila ku Brazil; kilasi ya Sukulu ya Alengezi a Ufumu ku Malawi

ZOFUNIKA KUSINKHA-SINKHA: Ngati ndinu mbeta, mungacite ciani kuti umbeta wanu ukhale waphindu?

Kodi anthu mu mpingo angacite ciani kuti alimbikitse na kuthandiza aja amene ni mbeta?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani