LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb19 June tsa. 6
  • “Musamade Nkhawa ndi Kanthu Kalikonse”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Musamade Nkhawa ndi Kanthu Kalikonse”
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Nkhani Zofanana
  • Tulilani Yehova Nkhawa Zanu Zonse
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
  • “Mtendele wa Mulungu ... Umaposa Kuganiza Mozama Kulikonse”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
  • Pemphelo—Kodi Lingakuthandizeni Bwanji?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • “Ine Ndidzakhala Nawe Polankhula”
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
mwb19 June tsa. 6

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | AFILIPI 1-4

“Musamade Nkhawa ndi Kanthu Kalikonse”

4:6, 7

Mlongo apemphela ndiyeno pambuyo pake mtima wake ukhala pansi
  • Pemphelo ndiye mankhwala a nkhawa

  • Ngati tipemphela tili na cikhulupililo, Yehova adzatipatsa mtendele umene “umaposa kuganiza mozama kulikonse”

  • Ngakhale tithedwe nzelu na mavuto amene takumana nawo, Yehova angatithandize kuwapilila. Angatithandize m’njila imene sitinali kuyembekezela.—1 Akor. 10:13

Ni zinthu ziti zimene zimanipatsa nkhawa mu umoyo wanga?

Ningaonetse bwanji kuti nimadalila kwambili Yehova?

Mlongo ali na nkhawa ya mmene adzalipilila mabilu; mlongo wacikulile apemphela pamene akudwazika mwamuna wake ku cipatala; makolo akukangana, ndipo ana aona na kumva zimenezo
    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani