LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb19 July tsa. 4
  • July 15-21

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • July 15-21
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
mwb19 July tsa. 4

July 15-21

2 ATESALONIKA 1-3

  • Nyimbo 67 na Pemphelo

  • Mawu Oyamba (3 min. olo kucepelapo)

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Wosamvela Malamulo Aonekela”: (10 min.)

    • [Tambitsani vidiyo yakuti Mfundo Zokhudza Buku la 2 Atesalonika.]

    • 2 Ates. 2:6-8—“Wosamvela malamuloyo,” amene alipo kale, adzaonekela (it-1 972-973)

    • 2 Ates. 2:9-12—Anthu amene amasoceletsedwa na “wosamvela malamulo,” adzaweluzidwa (it-2 245 ¶7)

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (8 min.)

    • 2 Ates. 1:7, 8—Kodi Yesu pamodzi na angelo adzaonekela motani “m’moto walawi-lawi”? (it-1 834 ¶5)

    • 2 Ates. 2:2—Kodi Paulo anatanthauza ciani pamene anakamba mawu akuti “mawu ouzilidwa”? (it-1 1206 ¶4)

    • Kodi imwe pacanu, kuŵelenga Baibo kwa wiki ino kwakuphunzitsani ciani za Yehova?

    • Ni cuma ca kuuzimu cina citi cimene mwapeza pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino?

  • Kuŵelenga Baibo: (4 min. olo kucepelapo) 2 Ates. 1:1-12 (th phunzilo 10)

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Wobwelelako Woyamba: (5 min.) Tambitsani na kukambilana vidiyoyi.

  • Ulendo Wobwelelako Woyamba: (3 min. olo kucepelapo) Seŵenzetsani makambilano acitsanzo. (th phunzilo 6)

  • Ulendo Wobwelelako Woyamba: (4 min. olo kucepelapo) Yambani na makambilano acitsanzo, ndiyeno gaŵilani buku yakuti Zimene Baibulo Ingatiphunzitse. (th phunzilo 12)

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

  • Nyimbo 61

  • Kodi Munaleka Kusangalala na Ulaliki?: (15 min.) Tambitsani vidiyo yakuti Wonjezelani Cangu pa Utumiki Wanu—Motani?

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 75

  • Kubwelelamo na Kuchulako za Wiki Yotsatila (3 min.)

  • Nyimbo 111 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani