LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb20 March tsa. 3
  • March 9-15

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • March 9-15
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
mwb20 March tsa. 3

March 9-15

GENESIS 24

  • Nyimbo 132 na Pemphelo

  • Mawu Oyamba (1 min.)

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Mkazi wa Isaki”: (10 min.)

    • Gen. 24:2-4—Abulahamu anatumiza mtumiki wake kukafunila Isaki mkazi pakati pa anthu olambila Yehova (wp16.3 14 ¶3)

    • Gen. 24:11-15—Mtumiki wa Abulahamu anakumana na Rabeka pa citsime (wp16.3 14 ¶4)

    • Gen. 24:58, 67—Rabeka anavomela kukwatiwa kwa Isaki (wp16.3 14 ¶6-7)

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (10 min.)

    • Gen. 24:19, 20—Kodi tiphunzilapo ciani pa zimene Rabeka anacita zochulidwa m’mavesiwa? (wp16.3 12-13)

    • Gen. 24:65—N’cifukwa ciani Rabeka anaphimba kumutu kwake? Nanga zimenezi zitiphunzitsa ciani? (wp16.3 15 ¶3)

    • Pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino, ni mfundo yopindulitsa iti imene munapeza yokhudza Yehova Mulungu, ulaliki, kapena mbali ina iliyonse?

  • Kuŵelenga Baibo: (4 min. olo kucepelapo) Gen. 24:1-21 (th phunzilo 2)

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Woyamba: (4 min.) Kukambilana. Tambitsani vidiyoyi, ndiyeno funsani omvetsela mafunso otsatilawa: Kodi wofalitsa waseŵenzetsa bwanji mafunso mwaluso? Nanga kodi wofalitsayu wayankha bwanji pamene mwininyumba wapeleka yankho yake ponena za Yesu?

  • Ulendo Woyamba: (2 min. olo kucepelapo) Seŵenzetsani makambilano acitsanzo. (th phunzilo 1)

  • Ulendo Woyamba: (3 min. olo kucepelapo) Mukayamba makambilano acitsanzo, mwininyumba akambe mawu ofala kwanuko ofuna kukanila ulaliki. Koma mwaluso, loŵelani pa mawu amenewo. (th phunzilo 12)

  • Kuitanila Anthu ku Cikumbutso: (3 min. olo kucepelapo) Yambani na makambilano acitsanzo. Mwininyumba aonetse cidwi. Kenako chulani na kukambilana vidiyo yakuti Kukumbukila Imfa ya Yesu. (Koma musaitambitse) (th phunzilo 11)

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

  • Nyimbo 25

  • Kampeni Yomemeza Anthu ku Cikumbutso Idzayamba pa Ciŵelu, March 14: (8 min.) Kukambilana. Gaŵilani aliyense m’gulu kapepa koitanila anthu ku cikumbutso na kukambilana zimene zilimo. Tambitsani na kukambilana vidiyo ya ulaliki wacitsanzo. Fotokozani makonzedwe a pa mpingo panu okafolela magawo.

  • “Kodi Nidzaitanila Ndani?”: (7 min.) Kukambilana.

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 107

  • Mawu Othela (3 min. olo kucepelapo)

  • Nyimbo 9 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani