LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb20 June tsa. 3
  • June 8-14

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • June 8-14
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
mwb20 June tsa. 3

June 8-14

GENESIS 46-47

  • Nyimbo 86 na Pemphelo

  • Mawu Oyamba (1 min.)

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Thandizo la Cakudya pa Nthawi ya Njala”: (10 min.)

    • Gen. 47:13—M’dziko la Iguputo komanso la Kanani munagwa njala yaikulu (w87 5/1 15 ¶2)

    • Gen. 47:16, 19, 20—Aiguputo anafunika kudzimana zinthu zina kuti akhalebe na moyo

    • Gen. 47:23-25—Khama n’lofunika kuti tipindule na cakudya cauzimu ca mwana alilenji cimene tili naco masiku ano (kr 234-235 ¶11-12)

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (10 min.)

    • Gen. 46:4—Kodi Yehova anatanthauza ciani pamene anauza Yosefe kuti ni amene ‘adzatseka maso’ a Yakobo? (it-1 220 ¶1)

    • Gen. 46:26, 27—Kodi ni anthu angati a m’nyumba ya Yakobo amene analoŵa mu Iguputo? (nwtsty mfundo younikila pa Mac. 7:14)

    • Pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino, ni mfundo yopindulitsa iti imene munapeza yokhudza Yehova Mulungu, ulaliki, kapena mfundo ina iliyonse?

  • Kuŵelenga Baibo: (4 min. olo kucepelapo) Gen. 47:1-17 (th phunzilo 10)

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Woyamba: (4 min.) Kukambilana. Tambitsani vidiyoyi, ndiyeno funsani omvetsela mafunso aya: Kodi wofalitsa uja waseŵenzetsa bwanji mafunso mwaluso? Kodi wamveketsa bwanji mfundo ya palemba?

  • Ulendo Woyamba: (3 min. olo kucepelapo) Yambani na makambilano acitsanzo, ndiyeno gaŵilani cofalitsa ca mu Thuboksi yathu. (th phunzilo 3)

  • Ulendo Woyamba: (3 min. olo kucepelapo) Yambani na makambilano acitsanzo, ndiyeno gaŵilani buku lakuti Zimene Baibulo Ingatiphunzitse, ndipo yambitsani phunzilo la Baibo m’mutu 9. (th phunzilo 14)

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

  • Nyimbo 96

  • Musaleke Kuŵelenga na Kusunga Zikumbutso za Yehova: (15 min.) Tambitsani vidiyo yakuti, Muziyamikila Zikumbutso za Yehova. Limbikitsani onse kuti apitilize kuŵelenga Mawu a Mulungu komanso kupindula na cakudya cauzimu cimene tili naco.—Yes. 25:6; 55:1; 65:13; Mat. 24:45.

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 118

  • Mawu Othela (3 min. olo kucepelapo)

  • Nyimbo 109 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani