LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb20 September tsa. 2
  • September 7-13

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • September 7-13
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
mwb20 September tsa. 2

September 7-13

EKSODO 23-24

  • Nyimbo 34 na Pemphelo

  • Mawu Oyamba (1 min.)

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU

  • “Usatsatile Khamu la Anthu”: (10 min.)

    • Eks. 23:1—“Usafalitse nkhani yabodza” (w18.08 4 ¶7-8)

    • Eks. 23:2—Usalole khamu la anthu kukunyengelela kucita zoipa (it-1 11 ¶3)

    • Eks. 23:3—Usakondele anthu ena (it-1 343 ¶5)

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (10 min.)

    • Eks. 23:9—Kodi Yehova anawauza ciani Aisiraeli pankhani yocitila cifundo alendo? (w16.10 9 ¶4)

    • Eks. 23:20, 21—Kodi pali umboni wotani wotsimikizila kuti mngelo amene akuchulidwa palembali ni Mikayeli? (it-2 393)

    • Pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino, ni mfundo yopindulitsa iti imene munapeza yokhudza Yehova, ulaliki, kapena mfundo ina iliyonse?

  • Kuŵelenga Baibo: (4 min. olo kucepelapo) Eks. 23:1-19 (th phunzilo 5)

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Woyamba: (4 min.) Kukambilana. Tambitsani vidiyoyi. Ndiyeno funsani omvetsela: Kodi wofalitsayo wacita ciani kuti asasokoneze ulaliki pamene mwininyumba wapeleka yankho yolakwika? Akanafuna, kodi wofalitsayo akanacita ciani kuti agaŵile Nsanja ya Mlonda No. 3 2020?

  • Ulendo Woyamba: (3 min. olo kucepelapo) Yambani na makambilano acitsanzo. Kenako chulani na kukambilana vidiyo yakuti N’cifukwa Ciani Muyenela Kuphunzila Baibulo? (koma musaitambitse) (th phunzilo 1)

  • Nkhani: (5 min. olo kucepelapo) w16.05 30-31—Mutu: Kodi Mkhristu Angadziŵe Bwanji Ngati N’zoyenela Kupeleka Ndalama Yoyamikila Wogwila Nchito wa Boma? ( th phunzilo 14)

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

  • Nyimbo 124

  • “Pewani Kufalitsa Nkhani Zabodza”: (15 min.) Kukambilana. Tambitsani vidiyo yatukadoli yakuti Kodi Ningakanize Bwanji Mijedo?

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min. olo kucepelapo) jy mutu 131

  • Mawu Othela (3 min. olo kucepelapo)

  • Nyimbo 145 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani