LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb20 October tsa. 7
  • October 26–November 1

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • October 26–November 1
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2020
mwb20 October tsa. 7

October 26–November 1

EKSODO 37-38

  • Nyimbo 43 na Pemphelo

  • Mawu Oyamba (1 min.)

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Maguwa Ansembe a pa Cihema Komanso Nchito Yawo pa Kulambila Koona”: (10 min.)

    • Eks. 37:25—Guwa la nsembe zofukiza linali kukhala m’Malo Oyela (it-1 82 ¶3)

    • Eks. 37:29—Zofukiza zopatulika zinali zosakanizidwa mwaluso (it-1 1195)

    • Eks. 38:1—Guwa la nsembe zopseleza linali kukhala m’bwalo la cihema (it-1 82 ¶1)

  • Kufufuza Cuma ca Kuuzimu: (10 min.)

    • Eks. 37:1, 10, 25—N’cifukwa ciani mthethe unali mtengo wabwino kwambili wopangila zinthu za pa cihema? (it-1 36)

    • Eks. 38:8—Kodi magalasi odziyang’anila akale anali osiyana bwanji ndi a masiku ano? (w15 4/1 15 ¶4)

    • Pa kuŵelenga Baibo kwa wiki ino, ni mfundo yopindulitsa iti imene munapeza yokhudza Yehova, ulaliki, kapena mfundo ina iliyonse?

  • Kuŵelenga Baibo: (4 min. olo kucepelapo) Eks. 37:1-24 (th phunzilo 5)

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Ulendo Woyamba: (3 min. olo kucepelapo) Mukayamba makambilano acitsanzo, mwininyumba akambe mawu ofala kwanuko ofuna kukanila ulaliki. Koma mwaluso, loŵelani pa mawu amenewo. (th phunzilo 3)

  • Ulendo Wobwelelako: (4 min. olo kucepelapo) Yambani na makambilano acitsanzo. Ndiyeno gaŵilani magazini yatsopano imene iyankha funso limene mwininyumba wafunsa. (th phunzilo 12)

  • Phunzilo la Baibo: (5 min. olo kucepelapo) bhs 199 ¶8-9 (th phunzilo 7)

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

  • Nyimbo 67

  • Zofunikila za Mpingo: (5 min.)

  • “Kampeni Yapadela Yolengeza za Ufumu wa Mulungu mu November”: (10 min.) Kukambilana. Tambitsani na kukambilana vidiyo ya ulendo woyamba ya mwezi wa November.

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo: (30 min. olo kucepelapo) jy mutu 138

  • Mawu Othela (3 min. olo kucepelapo)

  • Nyimbo 22 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani