LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb21 May tsa. 8
  • May 31–June 6

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • May 31–June 6
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
mwb21 May tsa. 8

May 31–June 6

DEUTERONOMO 1–2

  • Nyimbo 125 na Pemphelo

  • Mawu Oyamba (Mph. 1)

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Mulungu Ndiye Woweluza”: (Mph. 10)

  • Kufufuza Cuma Cauzimu: (Mph. 10)

    • Deut. 1:19; 2:7—Kodi Yehova anawasamalila bwanji anthu ake pa ulendo wawo wa zaka 40 wodutsa “m’cipululu cacikulu ndi cocititsa mantha”? (w13 9/15 9 ¶9

    • Pa kuŵelenga Baibo kwa mlungu uno, ni mfundo yopindulitsa iti imene munapeza yokhudza Yehova, ulaliki, kapena mfundo ina iliyonse?

  • Kuŵelenga Baibo: (Mph. 4) Deut. 1:1-18 (th phunzilo 10)

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Ulendo Woyamba: (Mph. 3) Mukayamba makambilano acitsanzo, mwininymba akambe mawu ofala kwanuko ofuna kukanila ulaliki, koma mwaluso loŵelani pa mawu amenewo. (th phunzilo 16)

  • Ulendo Wobwelelako: (Mph. 4) Yambani na makambilano acitsanzo. Gaŵilani mwininyumba kapepala koitanila anthu ku misonkhano. Ndiyeno chulani za vidiyo yakuti, N’ciani Cimacitika ku Nyumba ya Ufumu? (koma musaitambitse). (th phunzilo 11)

  • Nkhani: (Mph. 5) w13 8/1 14 ¶7—Mutu: Pewani Kukamba Kapena Kumvetsela Mawu Ofooketsa. (th phunzilo 13)

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

  • Nyimbo 30

  • “Khalanibe Wokonzeka m’Ndime Ino Yothela ya ‘Masiku Otsiliza’”: (Mph. 15) Nkhani yokambilana yokambidwa na mkulu. Onetsani vidiyo yakuti Kodi Mwakonzekela Tsoka la Zacilengedwe?. Fotokozani zikumbutso zocokela ku ofesi ya nthambi komanso za bungwe la akulu ngati zilipo.

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo: (Mph. 30) lfb phunzilo 39

  • Mawu Othela (Mph. 3)

  • Nyimbo 39 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani