LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb21 July tsa. 10
  • August 9-15

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • August 9-15
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
mwb21 July tsa. 10

August 9-15

DEUTERONOMO 24-26

  • Nyimbo 137 na Pemphelo

  • Mawu Oyamba (Mph. 1)

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Mmene Cilamulo Cinaonetsela Kuti Yehova Amawadela Nkhawa Akazi”: (Mph. 10)

  • Kufufuza Cuma Cauzimu: (Mph. 10)

    • Deut. 24:1—N’cifukwa ciani sitiyenela kuganiza kuti Cilamulo ca Mose cinapangitsa kuti cikhale cosavuta kwa mwamuna kusudzula mkazi wake? (it-1 640 ¶5)

    • Pa kuŵelenga Baibo kwa mlungu uno, ni mfundo yopindulitsa iti imene munapeza yokhudza Yehova, ulaliki, kapena mfundo ina iliyonse?

  • Kuŵelenga Baibo: (Mph. 4) Deut. 26:4-19 (th phunzilo 10)

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Ulendo Woyamba: (Mph. 3) Mukayamba na makambilano acitsanzo, mwininyumba akambe mawu ofala kwanuko ofuna kukanila ulaliki, koma mwaluso loŵelani pa mawu amenewo. (th phunzilo 1)

  • Ulendo Wobwelelako: (Mph.4) Yambani na makambilano acitsanzo. Ndiyeno, gaŵilani cofalitsa ca m’Thuboksi yathu. (th phunzilo 2)

  • Nkhani: (Mph. 5) w19.06 23-24 ¶13-16—Mutu: Kodi Tingawatonthoze Bwanji na Kuwalimbikitsa Anthu Amene Anafedwa Mnzawo wa M’cikwati? (th phunzilo 20)

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

  • Nyimbo 100

  • “Akazi Acikulile Muzicita Nawo Zinthu Monga Amayi Anu, Akazi Acitsikana Monga Azilongosi Anu”: (Mph. 15) Kukambilana. Onetsani vidiyo yakuti, Onetsani Cikondi Cosatha Mumpingo—Kwa Akazi Amasiye ndi Ana Amasiye.

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo: (Mph. 30) lfb phunzilo 50

  • Mawu Othela (Mph. 3)

  • Nyimbo 150 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani