LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb21 September tsa. 6
  • September 20-26

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • September 20-26
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
mwb21 September tsa. 6

September 20-26

YOSWA 3-5

  • Nyimbo 65 na Pemphelo

  • Mawu Oyamba (Mph. 1)

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Yehova Amatidalitsa Ngati Ticita Zinthu Zoonetsa Cikhulupililo”: (Mph. 10)

  • Kufufuza Cuma Cauzimu: (Mph. 10)

    • Yos. 5:14, 15—Kodi timakhulupilila kuti “kalonga wa gulu lankhondo la Yehova” ndani? (w04 12/1 9 ¶2)

    • Pa kuŵelenga Baibo kwa mlungu uno, ni mfundo yopindulitsa iti imene munapeza yokhudza Yehova, ulaliki, kapena mfundo ina iliyonse?

  • Kuŵelenga Baibo: (Mph. 4) Yos. 3:1-13 (th phunzilo 10)

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • “Wonjezelani Cimwemwe Canu mu Ulaliki— Seŵenzetsani Zida Zofufuzila”: (Mph. 10) Kukambilana. Onetsani vidiyo yakuti Pezani Cimwemwe pa Nchito Yopanga Ophunzila—Landilani Thandizo la Yehova—Zida Zofufuzila.

  • Phunzilo la Baibo: (Mph. 5) lffi phunzilo 01, ndime yoyamba na mfundo 1-2 (th phunzilo 15)

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

  • Nyimbo 96

  • Zofunikila za Mpingo: (Mph. 15)

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo: (Mph. 30) lfb, phunzilo 56

  • Mawu Othela (Mph. 3)

  • Nyimbo 94 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani