LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb22 July tsa. 8
  • August 1-7

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • August 1-7
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
mwb22 July tsa. 8

August 1-7

1 MAFUMU 1-2

  • Nyimbo 98 na Pemphelo

  • Mawu Oyamba (Mph. 1)

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Kodi Mumaphunzilapo Kanthu pa Zolakwa Zanu?”: (Mph. 10)

  • Kufufuza Cuma Cauzimu: (Mph. 10)

    • 1 Maf. 2:37, 41-46—Kodi tiphunzilapo ciyani pa colakwa ca Simeyi? (w05 7/1 30 ¶1)

    • Pa kuŵelenga Baibo kwa mlungu uno, ni mfundo yopindulitsa iti imene munapeza yokhudza Yehova, ulaliki, kapena mfundo ina iliyonse?

  • Kuŵelenga Baibo: (Mph. 4) 1 Maf. 1:28-40 (th phunzilo 2)

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Ulendo Woyamba: (Mph. 3) Makambilano anu atsamile pa mfundo yaikulu ya makambilano acitsanzo. M’gaŵileni kakhadi koloŵela pa jw.org. (th phunzilo 11)

  • Ulendo Wobwelelako: (Mph. 4) Makambilano anu atsamile pa mfundo yaikulu ya makambilano acitsanzo. Chulani za vidiyo yakuti N’ciani Cimacitika ku Nyumba ya Ufumu? (koma musaitambitse). Kenako itanilani mwininyumba ku misonkhano. (th phunzilo 20)

  • Nkhani: (Mph. 5) km 1/15 2 ¶1-3—Mutu: Phunzilani kwa Ofalitsa Aluso mu Ulaliki. (th phunzilo 13)

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

  • Nyimbo 84

  • “Dziikileni Zolinga za Caka ca Utumiki Catsopano—Funsilani Kuloŵa Sukulu ya Alengezi a Ufumu”: (Mph. 7) Kukambilana. Onetsani vidiyo yakuti Loŵani pa Khomo la Zocita Zambili m’Cikhulupililo—Funsilani Kuloŵa Sukulu ya Alengezi a Ufumu.

  • “Dziikileni Zolinga za Caka ca Utumiki Catsopano—Dzipelekeni Kuthandiza pa Nchito Zomanga za Gulu”: (Mph. 8) Kukambilana. Onetsani vidiyo yakuti Loŵani pa Khomo la Zocita Zambili m’Cikhulupililo—Dzipelekeni Kuthandiza pa Nchito Zomanga za Gulu.

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo: (Mph. 30) lff phunzilo 14

  • Mawu Othela (Mph. 3)

  • Nyimbo 24 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani