LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb23 January tsa. 12
  • February 13-19

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • February 13-19
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
mwb23 January tsa. 12

February 13-19

1 MBIRI 13-16

  • Nyimbo 123 na Pemphelo

  • Mawu Oyamba (Mph. 1)

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Kutsatila Malangizo Kumacititsa Kuti Zinthu Zitiyendele Bwino”: (Mph. 10)

  • Kufufuza Cuma Cauzimu: (Mph. 10)

    • 1 Mbiri 16:31—N’cifukwa ciyani Alevi anaimba kuti, “Yehova wakhala mfumu”? w14 1/15 10 ¶14)

    • Pa kuŵelenga Baibo kwa mlungu uno, ni mfundo yopindulila iti imene munapeza yokhudza Yehova, ulaliki, kapena mfundo ina iliyonse?

  • Kuŵelenga Baibo: (Mph. 4) 1 Mbiri 13:1-14 (th phunzilo 11)

CITANI KHAMA PA ULALIKI

  • Ulendo Woyamba: (Mph. 3) Makambilano anu atsamile pa mfundo yaikulu ya makambilano acitsanzo. Mukayamba, mwininyumba akambe mawu ofala kwanuko ofuna kukanila ulaliki. Koma mwaluso loŵelani pa mawu amenewo. (th phunzilo 18)

  • Ulendo Wobwelelako: (Mph. 4) Makambilano anu atsamile pa mfundo yaikulu ya makambilano acitsanzo. M’gaŵileni cofalitsa ca m’Thuboksi yathu. (th phunzilo 7)

  • Nkhani: (Mph. 5) w16.01 13-14 ¶7-10—Mutu: “Cikondi Cimene Khristu Ali Naco Cimatikakamiza.”—2 Akor. 5:14. (th phunzilo 8)

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

  • Nyimbo 86

  • Khala Bwenzi la Yehova—Uzimvetsela Mwachelu pa Misonkhano: (Mph. 5) Kukambilana. Tambitsani vidiyoyi. Ndiyeno ngati n’kotheka funsani mafunso ana amene munawasankhilatu. Afunseni kuti: N’cifukwa ciyani tiyenela kumvetsela mwachelu pa misonkhano? N’ciyani cingakuthandize kucita zimenezi?

  • Zofunikila za Mpingo: (Mph. 10)

  • Phunzilo la Baibo la Mpingo: (Mph. 30) lff phunzilo 37 mfundo 6 cidule cake, kubweleza, na colinga

  • Mawu Othela (Mph. 3)

  • Nyimbo 21 na Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani