LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w20 January tsa. 32
  • Zina Zimene Zilipo Pa Jw.Org

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zina Zimene Zilipo Pa Jw.Org
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2020
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2020
w20 January tsa. 32

Zina Zimene Zilipo Pa Jw.Org

BAIBULO LIMASINTHA ANTHU

Moyo Wanga Unkangoipilaipilabe

Solomone anali kuganiza kuti akasamukila ku America, azikakhala na umoyo wabwino. M’malo mwake, kumeneko anayamba kugwilitsila nchito mankhwala osokoneza bongo ndipo anamangidwa. Kodi n’ciani cinamuthandiza kuti asinthe umoyo wake?

Pitani pa jw.org ku Chichewa, pa mbali yakuti ZOKHUDZA IFE > ZOCHITIKA PA MOYO WA A MBONI ZA YEHOVA > BAIBULO LIMASINTHA ANTHU.

ZIMENE ACHINYAMATA AMAFUNSA

Ndingatani Ngati Anzanga Amandiona Kuti Ndine Wotsalila?

Kodi mumaona kuti n’zoyenela kucita zinthu kuti mufanane na anzanu omwe satsatila mfundo za makhalidwe abwino kapena mumaona kuti cofunika ni kungokhala mmene mulili?

Pitani pa jw.org ku Chichewa, pa mbali yakuti ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA > ACHINYAMATA > ZIMENE ACHINYAMATA AMAFUNSA.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani