LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb25 March tsa. 11
  • April 14-20

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • April 14-20
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku Misonkhano—2025
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku Misonkhano—2025
mwb25 March tsa. 11

APRIL 14-20

MIYAMBO 9

Nyimbo 56 ndi Pemphelo | Mawu Oyamba (Mph. 1)

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

1. Khalani Munthu Wanzelu, Osati Wonyoza

(Mph. 10)

Munthu wonyoza amakana uphungu wacikondi, ndipo amakwiyila munthu yemwe wamupatsa uphunguwo (Miy. 9:​7, 8a; w22.02 9 ¶4)

Munthu wanzelu amayamikila uphungu komanso yemwe wamupatsa uphunguwo (Miy. 9:8b, 9; w22.02 12 ¶12-14; w01-CN 5/15 30 ¶1-2)

Munthu wanzelu adzapeza mapindu, koma munthu wonyoza adzavutika (Miy. 9:12; w01-CN 5/15 30 ¶5)

Mlongo wacitsikana akumvetsela malangizo a mlongo wacikulile pamene akudya cakudya ku malo odyela.

2. Kufufuza Cuma Cauzimu

(Mph. 10)

  • Miy. 9:17​—Kodi “madzi akuba” n’ciyani? Nanga n’cifukwa ciyani “amatsekemela”? (w06-CN 9/15 17 ¶5)

  • Pa kuwelenga Baibulo kwa mlungu uno, munapeza mfundo zothandiza ziti zimene mungakonde kutifotokozelako?

3. Kuwelenga Baibulo

(Mph. 4) Miy. 9:​1-18 (th phunzilo 5)

CITANI KHAMA PA ULALIKI

4. Kubwelelako

(Mph. 4) KUNYUMBA NDI NYUMBA. Munthuyo anapezeka ku Cikumbutso. (lmd phunzilo 8 mfundo 3)

5. Kubwelelako

(Mph. 4) ULALIKI WAPOYELA. Pa ulendo wapita, munathandiza munthuyo kupeza malo a kufupi ndi kwawo kumene kudzacitikila Cikumbutso. (lmd phunzilo 7 mfundo 4)

6. Kubwelelako

(Mph. 4) ULALIKI WAMWAYI. Pa ulendo wapita, munathandiza wacibale wanu kupeza malo a kufupi ndi kwawo kumene kudzacitikila Cikumbutso. (lmd phunzilo 8 mfundo 4)

UMOYO WATHU WACIKHRISTU

Nyimbo 84

7. Kodi Mwayi wa Utumiki Umakupangitsani Kukhala Apadela?

(Mph. 15) Kukambilana.

Tambitsani VIDIYO. Kenako funsani omvela kuti:

  • Kodi mawu akuti “utumiki” amatanthauza ciyani?

  • Kodi anthu amene ali ndi maudindo mumpingo ayenela kudziona bwanji?

  • N’cifukwa ciyani kutumikila ena n’kofunika kwambili kuposa kukhala ndi maudindo?

8. Phunzilo la Baibulo la Mpingo

(Mph. 30) bt mutu 25 ¶5-7, bokosi pa tsa. 200

Mawu Othela (Mph. 3) | Nyimbo 42 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani