LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w22 August tsa. 32
  • Zina Zimene Zilipo Pa JW.ORG

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zina Zimene Zilipo Pa JW.ORG
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2022
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2022
w22 August tsa. 32

Zina Zimene Zilipo Pa JW.ORG

NKHANI ZOKHUDZA MBONI ZA YEHOVA

Tinasankha Kukhala Moyo Wosalira Zambiri

Madián na Marcela anapeza kungokhalila kugula zinthu komanso kukhala na nkhongole yaikulu, kunali kuwonjezela nkhawa mu umoyo wawo. Koma kuphunzitsa ena za Mulungu kunawabweletsela cimwemwe ceniceni.

NKHANI ZINA

Kodi Baibulo Lingakuthandizeni Pakachitika Ngozi Zam’chilengedwe?

Malangizo anzelu a m’Baibo angakuthandizeni ngozi ya zacilengedwe isanacite, ili mkati, komanso pambuyo pake.

MFUNDO ZOTHANDIZA MABANJA

Zimene Makolo Ayenera Kudziwa Zokhudza Kutumiza Mwana Kumalo Osamalira Ana Masana

Makolo asanatumize mwana kumalo osamalila ana masana, ayenela kuganizila ubwino komanso kuipa kwake. Mafunso a m’nkhani ino angakuthandizeni kudziŵa zimene zingathandize mwana wanu.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani