LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w16 February masa. 1-2
  • Zamkati

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zamkati
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2016
w16 February masa. 1-2

Zamkati

February 2016

© 2016 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

MLUNGU WA APRIL 4-10, 2016

3 Yehova Anamucha kuti “Bwenzi Langa”

MLUNGU WA APRIL 11-17, 2016

9 Tengelani Citsanzo ca Mabwenzi Apamtima a Yehova

Nkhanizi zidzatithandiza kulimbitsa ubwenzi wathu ndi Yehova Mulungu. M’nkhani yoyamba, tidzakambilana citsanzo ca Abulahamu. M’nkhani yaciŵili, tidzakambilana citsanzo ca Rute, Hezekiya, ndi Mariya mai a Yesu.

MLUNGU WA APRIL 18-24, 2016

14 Khalani Wokhulupilika kwa Yehova

MLUNGU WA APRIL 25, 2016–MAY 1, 2016

20 Tengelani Citsanzo ca Atumiki Okhulupilika a Yehova

M’nkhani ziŵilizi, tidzakambilana zocitika za m’Baibulo zokhudza Mfumu Davide ndi ena amene analiko m’nthawi yake. Pamene tikambilana zitsanzo zao, tidzaona zimene zingatithandize kukhalabe okhulupilika kwa Yehova ngakhale panthawi zovuta.

26 Mbili Yanga​—Yehova Wandidalitsa mu Utumiki Wake

30 Pitilizani Kutumikila Yehova Mwacimwemwe

CITHUNZI CA PACIKUTO:

BENIN

Ku mudzi wa Hetin, nyumba zambili anazimanga pamwamba pa mitengo kuti madzi asamaloŵe. Anthu amagwilitsila nchito mabwato aang’ono akafuna kuyenda ulendo waufupi. Ofalitsa 215 ndi apainiya 28 a m’mipingo itatu ya m’mudziwo, anasangalala kwambili pamene anthu 1,600 anapezeka pa Cikumbutso mu 2014

KULI ANTHU

10,703,000

OFALITSA

12,167

APAINIYA A NTHAWI ZONSE

1,492

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani