LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 55
  • Tidzapeza Moyo Wosatha!

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Tidzapeza Moyo Wosatha!
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Moyo Wosatha Watheka!
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nyimbo Yatsopano
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nyimbo Yatsopano
    Imbirani Yehova
  • Munapeleka Mwana Wanu Wobadwa Yekha
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 55

Nyimbo 55

Tidzapeza Moyo Wosatha!

(Yohane 3:16)

1. Onani m’maganizo

Anthuwo pamtendere

Zosautsa zathadi!

Palibe kulira.

(KOLASI)

Imbani mokondwa!

Ngakhale inunso

Patsikulo mudzati,

“Moyo wosathadi!”

2. Anthunso Okalamba

Adzakhala ’nyamata.

Mavutowa adzatha,

Anthu sadzalira.

(KOLASI)

Imbani mokondwa!

Ngakhale inunso

Patsikulo mudzati,

“Moyo wosathadi!”

3. Anthu’fe tidzakondwa

Poimbira Mulungu.

Nthawi zonse tidzati,

“Zikomo Yehova.”

(KOLASI)

Imbani mokondwa!

Ngakhale inunso

Patsikulo mudzati,

“Moyo wosathadi!”

(Onaninso Yobu 33:25; Sal. 72:7; Chiv. 21:4.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani