LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 37
  • Malemba Anauziridwa ndi Mulungu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Malemba Anauziridwa ndi Mulungu
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Malemba ni Ouzilidwa na Mulungu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Musalole Ciliconse Kukumanitsani Mphoto
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
  • “Onetsani Kuwala Kwanu”
    Imbirani Yehova
  • “Onetsani Kuwala Kwanu”
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Imbirani Yehova
sn nyimbo 37

Nyimbo 37

Malemba Anauziridwa ndi Mulungu

(2 Timoteyo 3:16, 17)

1. M’dzikoli, Mawu a M’lungu

Amatiunikira.

Tikawatsatira bwino,

Cho’nadi chitimasula.

2. Mawu ndi ouziridwa,

Amatiphunzitsadi.

Amawongoladi zinthu

Ndiponso kutilangiza.

3. Malemba akumwambawa,

Atidziwitsa M’lungu.

Ngati timawawerenga,

Tingadzapezedi mphoto.

(Onaninso Sal. 119:105; Miy. 4:13.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani