LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 46
  • Yehova ndi Mfumu Yathu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Yehova ndi Mfumu Yathu
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Yehova Ndiye Mfumu Yathu!
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Ufumu Ulamulila—Ubwele!
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Ufumu Ulamulila—Ubwele!
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • “Cimwemwe Cimene Yehova Amapeleka”
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
Imbirani Yehova
sn nyimbo 46

Nyimbo 46

Yehova ndi Mfumu Yathu

(Salmo 97:1)

1. Kondwa, lemekeza Yehova.

Kumwamba kulengeza chilungamo.

Titame Mulungu ndi nyimbo mokondwa

Pa ntchito zake zazikulu.

(KOLASI)

Kumwamba kukondwe, Dziko likondwere,

Chifukwa Yehova ndi Mfumu!

Kumwamba kukondwe, Dziko likondwere,

Chifukwa Yehova ndi Mfumu!

2. Nena za kukwezeka kwake,

Za kupulumutsa kwake kwamphamvu.

Yehova ndi Mfumu, Timutamandetu.

Tiyeni, tim’gwadire tonse.

(KOLASI)

Kumwamba kukondwe, Dziko likondwere,

Chifukwa Yehova ndi Mfumu!

Kumwamba kukondwe, Dziko likondwere,

Chifukwa Yehova ndi Mfumu!

3. Wakhazikitsatu Ufumu.

Waika Mwana wake pampandowo.

Milungu yonyenga ichite manyazi,

Ulemu wonse n’ngwa Yehova.

(KOLASI)

Kumwamba kukondwe, Dziko likondwere,

Chifukwa Yehova ndi Mfumu!

Kumwamba kukondwe, Dziko likondwere,

Chifukwa Yehova ndi Mfumu!

(Onaninso 1 Mbiri 16:9; Sal. 68:20; 97:6, 7.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani