LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • snnw nyimbo 139 tsa. 4
  • Aphunzitseni Kucilimika

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Aphunzitseni Kucilimika
  • Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Nkhani Zofanana
  • Aphunzitseni Kucilimika
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • Umoyo wa Mpainiya
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Moyo Ndi Wodabwitsa
    Imbirani Yehova
Onaninso Zina
Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
snnw nyimbo 139 tsa. 4

Nyimbo 139

Aphunzitseni Kucilimika

Yopulinta

(Mateyu 28:19, 20)

  1. Tikondwa kuphunzitsa anthu

    Okonda coonadi.

    Onani mmene akulila

    M’njila ya coonadi.

    (KOLASI)

    Yehova, mvelani pempho

    Lakuti muwasamale.

    Mu dzina la Yesu Khristu

    Tipemphela akhale ocilimika.

  2. Tinali kuwapemphelela

    M’mavuto awo onse.

    Tinali kuwasamalila

    Yehova ‘wadalitsa.

    (KOLASI)

    Yehova, mvelani pempho

    Lakuti muwasamale.

    Mu dzina la Yesu Khristu

    Tipemphela akhale ocilimika.

  3. Akhale odalila M’lungu,

    Na Mwana wake Yesu.

    Amvele ndipo apilile

    Tifuna apambane.

    (KOLASI)

    Yehova, mvelani pempho

    Lakuti muwasamale.

    Mu dzina la Yesu Khristu

    Tipemphela akhale ocilimika.

(Onaninso Luka 6:48; Mac. 5:42; Afil. 4:1.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani