LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 75
  • ‘Ine Nilipo, N’tumizeni!

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • ‘Ine Nilipo, N’tumizeni!
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • “Ine Ndilipo! Nditumizeni”
    Imbirani Yehova
  • Moyo Wosatha Watheka!
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Kukonzeka Kukalalikila
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Kukonzeka Kukalalikila
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 75

NYIMBO 75

‘Ine Nilipo, N’tumizeni!’

Yopulinta

(Yesaya 6:8)

  1. 1. Anthu anyoza Mulungu

    Aipitsa dzina lake.

    Zoipa zikacitika

    M’lungu ndiye wacititsa.

    Ndani adzaŵathandiza,

    Kudziŵa kuti si M’lungu?

    (KOLASI 1)

    “Ine M’lungu nitumeni,

    Nitamande dzina lanu.

    Ine nilipo n’tumizeni

    Yehova nitumeni.”

  2. 2. Ena sayopa Mulungu

    Amalambila mafano.

    Ndipo ena alambila

    Mafumu a dziko lawo.

    Ndani adzaŵacenjeza,

    Za nkhondo ya M’lungu wathu?

    (KOLASI 2)

    “Ine M’lungu nitumeni,

    nikaŵacenjeze onse.

    Ine nilipo n’tumizeni

    Yehova nitumeni.”

  3. 3. ‘Ofatsa adandaula

    Zoipa zaonjezeka.

    Na mtima wofunitsitsa

    Asakila coonadi.

    Ndani adzaŵathandiza,

    Kuti apeze co’nadi?

    (KOLASI 3)

    “Ine M’lungu nitumeni,

    Kuti nikaŵathandize.

    Ine nilipo n’tumizeni

    Yehova nitumeni.”

(Onaninso Sal. 10:4; Ezek. 9:4.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani