LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 92
  • Malo a Dzina Lanu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Malo a Dzina Lanu
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Malo Odziwika ndi Dzina Lanu
    Imbirani Yehova
  • M’patseni Ulemelelo Yehova
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Mvelani Pemphelo Langa Conde
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Mulungu Imvani Pemphero Langa
    Imbirani Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 92

NYIMBO 92

Malo a Dzina Lanu

Yopulinta

(1 Mbiri 29:16)

  1. 1. O Yehova, ni mwayi wathu,

    Kukumangilani nyumba!

    Ise pano tiipeleka,

    Kwa inu Mulungu wathu.

    Zilizonse tingapeleke

    Inde n’zanu kale zonse.

    Mphamvu, maluso, cuma cathu,

    Mokondwa tikupatsani.

    (KOLASI)

    Tipeleka malo aya,

    Conde alandileni.

    Achukitse dzina lanu

    Inde mutamandike.

  2. 2. Pamalo ano tiloleni

    Tikutamandeni M’lungu.

    Tidzasamalila nyumbayi,

    Tidziŵa kuti ni yanu.

    Ikhale umboni kwa onse,

    Wakuti ‘se ndise anu.

    Ulemelelo wa nyumbayi,

    Inde, ukwele kwa inu.

    (KOLASI)

    Tipeleka malo aya,

    Conde alandileni.

    Achukitse dzina lanu

    Inde mutamandike.

(Onaninso 1 Maf. 8:18, 27; 1 Mbiri 29:11-14; Mac. 20:24.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani