LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 117
  • Ubwino

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ubwino
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Tizichita Zinthu Zabwino
    Imbirani Yehova
  • Ubwino—Kodi tingalikulitse bwanji khalidwe limeneli?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2019
  • ‘Laŵani’ Ubwino wa Yehova—Motani?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2021
  • Lambirani Yehova Muli Achinyamata
    Imbirani Yehova
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 117

NYIMBO 117

Ubwino

Yopulinta

(2 Mbiri 6:41)

  1. 1. O Yehova M’lungu wathu,

    Ise mwatidalitsa.

    Ndinu wokhulupilika

    Wabwino m’zinthu zonse.

    Mwationetsa cifundo

    Cifukwa mutikonda.

    Tidzakutumikilani

    Nakukulambilani.

  2. 2. Tiona ubwino wanu

    Mwa anthu munasankha.

    Amalengeza uthenga

    Na kucita zabwino.

    Mwa akulu a mumpingo,

    Tipita patsogolo.

    Tipatseni mzimu wanu

    Tionetse ubwino.

  3. 3. Kwa abale athu onse,

    Tionetse ubwino.

    Tipempha mutithandize

    Kukonda athu onse.

    Ku mipingo na mabanja,

    Ndi kwa anansi athu,

    Tipempha thandizo lanu,

    Tionetse ubwino.

(Onaninso Sal. 103:10; Maliko 10:18; Agal. 5:22; Aef. 5:9.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani