LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb16 February tsa. 6
  • Zimene Tikuphunzila m’Buku la Nehemiya

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zimene Tikuphunzila m’Buku la Nehemiya
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Nkhani Zofanana
  • Mwapatulidwa
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2013
  • Mpanda Wa Yerusalemu
    Buku Langa La Nkhani Za M’baibo
  • Mpanda wa Yerusalemu Umangidwanso
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
mwb16 February tsa. 6

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | NEHEMIYA 12–13

Zimene Tikuphunzila m’Buku la Nehemiya

Nehemiya anateteza kulambila koona ndi mtima wonse

13:4-9, 15-21, 23-27

Nehemiya akuponya katundu wa Tobia kunja kwa cipinda codyelamo
  • Mkulu wa ansembe Eliyasibu, analola Tobia munthu wosakhulupilila Mulungu ndi wotsutsa kumuuza zocita

  • Eliyasibu anakonzela Tobia malo m’cipinda codyelamo pakacisi

  • Nehemiya anaponya katundu yense wa Tobia kunja kwa cipinda codyelamo, anayeletsa cipindaco ndi kuyamba kucigwilitsila nchito moyenelela

  • Nehemiya anapitilizabe kuyeletsa mzinda wa Yerusalemu

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani