LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb16 May tsa. 3
  • Yehova Amakondwela Tikamapemphelela Ena

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Yehova Amakondwela Tikamapemphelela Ena
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
  • Nkhani Zofanana
  • Limbikitsani Ena ndi Mau Abwino
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Msonkhano (2016)
mwb16 May tsa. 3

CUMA COPEZEKA M’MAU A MULUNGU | YOBU 38-42

Yehova Amakondwela Tikamapemphelela Ena

Yehova anafuna kuti Yobu apemphelele Elifazi, Bilidadi, ndi Zofari

42:7-10

Elifazi, Bilidadi, ndi Zofari akupeleka nsembe yopseleza pamene Yobu akuwapemphelela
  • Yehova anauza Elifazi, Bilidadi ndi Zofari kuti apeleke nsembe yopseleza

  • Yobu anali kufunika kupemphelela anzake atatu

  • Yobu anadalitsidwa atapemphelela anzakewo

Yehova anadalitsa Yobu kwambili cifukwa ca cikhulupilililo cake ndi kupilila

42:10-17

  • Yobu wacilitsidwa matenda ake

    Yehova anathetsa mavuto a Yobu, ndipo anamucilitsa matenda ake

  • Yobu atonthozedwa ndi ena

    Yobu anatonthozedwa ndi anzake komanso acibale ake pa mavuto amene anakumana nao

  • Gulu la nkhosa

    Yehova anabwezeletsa cuma cimene Yobu anali naco kuwilikiza kaŵili

  • Yobu ndi mkazi wake ali pamodzi ndi ana ao

    Yobu ndi mkazi wake anakhalanso ndi ana ena 10

  • Yobu ndi mkazi wake ali pamodzi ndi acibale ao ena

    Yobu anakhala ndi moyo zaka zina 140, ndipo anali ndi mwai woona mbadwo wacinai wa mzele wake wobadwila

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani