LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb23 November tsa. 5
  • Musawasiye Konse Alambili Anzanu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Musawasiye Konse Alambili Anzanu
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
  • Nkhani Zofanana
  • “Yembekezela Yehova”
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2022
  • Kodi Yobu Anali Ndani?
    Maphunzilo Amene Tingatengemo m’Baibo
  • Kodi Mukukumbukila?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2022
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
mwb23 November tsa. 5

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Musawasiye Konse Alambili Anzanu

Acibale a Yobu analeka kuyanjana naye (Yobu 19:13)

Ngakhale ana aang’ono komanso anchito ake analeka kumulemekeza (Yobu 19:​16, 18)

Ngakhalenso mabwenzi ake apamtima anamuukila (Yobu 19:19)

Mwamuna na mkazi wake akuthandiza mlongo amene akuvutika. Mwacifundo, mkazi akumvetsela mlongoyo pamene mwamuna wake akumukonzela khichini.

DZIFUNSENI KUTI, Ningaonetse bwanji kuti nimaŵakonda abale na alongo amene akukumana na mavuto?—Miy. 17:17; w22.01 16 ¶9; w21.09 30 ¶16; w90 9/1 22 ¶20.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani