LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mfundo ya Kumapeto

^ [1] (ndime 3) Abale ndi alongo ena amalephela kufika pamisonkhano pa zifukwa zina zomveka. Mwacitsanzo, ena akudwala matenda aakulu. Abale ndi alongonu, dziŵani kuti Yehova amamvetsa mavuto amene mukukumana nao ndipo amayamikila zonse zimene mumacita kuti mum’lambile. Akulu angawathandize anthu amenewa kuti azimvetsela misonkhano. Angacite zimenezi mwa kulumikiza misonkhano kudzela pa foni kapena kuwajambulila misonkhanoyo.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani