Mawu Amunsi
a Ngakhale kuti anthu ena amakamba kuti mbali zina za Baibo zimatsutsana, zimenezo zilibe umboni. Onani mutu 7 wa buku lakuti Baibulo—Kodi Ndilo Mau a Mulungu kapena a Munthu? lolembedwa ndi Mboni za Yehova.
a Ngakhale kuti anthu ena amakamba kuti mbali zina za Baibo zimatsutsana, zimenezo zilibe umboni. Onani mutu 7 wa buku lakuti Baibulo—Kodi Ndilo Mau a Mulungu kapena a Munthu? lolembedwa ndi Mboni za Yehova.